Kodi ndidzadyanso ine?

Ngati muli ngati ambiri mwa ife, ndiye kuti mwina munaona kale kuti dzikoli ndilodzaza ndi abambo ndi amayi amene akukhala mu nyengo ya zovuta, kuvutika tsiku ndi tsiku kungofuna kuti akhale moyo ndi kupeze chakudya komanso kokhala ndi banja lawo. Funso lomwe amadzifunsa silokuti “kodi ndidya chani madzulo ano?”, koma lokuti “Kodi ndidzadyanso ine?”

Kulembetsa email

Sign up for the TWR360 Newsletter

Access updates, news, Biblical teaching and inspirational messages from powerful Christian voices.

Zikomo polembetsa kuti muzilandira zizidziwiso kuchokera ku TWR360

Zina zofunikira zikusowekera